YouVersion Logo
Search Icon

Genesis 19:16

Genesis 19:16 CCL

Koma Loti ankakayikabe. Koma Yehova anawachitira chifundo motero kuti anthu aja anagwira mkazi wake ndi ana ake aakazi aja nawatsogolera bwinobwino kuwatulutsa mu mzindawo.

Free Reading Plans and Devotionals related to Genesis 19:16