YouVersion Logo
Search Icon

Genesis 18:23-24

Genesis 18:23-24 CCL

Kenaka Abrahamu anasendera kufupi ndi Iye nati, “Kodi mudzawonongera kumodzi wolungama ndi woyipa? Nanga bwanji patakhala anthu makumi asanu olungama mu mzindamo? Kodi mudzawonongadi onse osausiyako mzindawo chifukwa cha anthu makumi asanu olungama omwe ali mʼmenemo?

Free Reading Plans and Devotionals related to Genesis 18:23-24