YouVersion Logo
Search Icon

Genesis 16:11

Genesis 16:11 CCL

Mngelo wa Yehova uja anamuwuzanso kuti, “Ndiwe woyembekezera ndipo udzabala mwana wamwamuna. Udzamutcha dzina lake Ismaeli, pakuti Yehova wamva kulira chifukwa cha kuzunzika kwako.

Free Reading Plans and Devotionals related to Genesis 16:11