YouVersion Logo
Search Icon

Genesis 15:5

Genesis 15:5 CCL

Yehova anapita naye Abramu panja nati, “Tayangʼana kumwambaku, ndipo chifukwa cha chimenechi uwerenge nyenyezi ngati ungathe kuziwerenga.” Ndipo anamuwuza kuti, “Ndi mmene adzakhalire ana ako ndi zidzukulu zako.”

Free Reading Plans and Devotionals related to Genesis 15:5