Bible App logo
Search Icon

Ezekieli 7:9

Ezekieli 7:9 CCL

Ine sindidzakumvera chisoni kapena kukuleka. Ndidzakulanga malingana ndi ntchito zako ndiponso chifukwa cha miyambo yako yonyansa pakati pako. ‘Pamenepo udzadziwa kuti Ine Yehova ndine amene ndimakantha.’