Ezekieli 7:27
Ezekieli 7:27 CCL
Mfumu idzalira, kalonga adzagwidwa ndi mantha. Manja a anthu a mʼdzikomo azidzangonjenjemera ndi mantha. Ine ndidzawalanga molingana ndi machitidwe awo, ndipo ndidzawaweruza molingana ndi momwe anaweruzira anzawo. Choncho adzadziwa kuti Ine ndine Yehova.”

