Bible App logo
Search Icon

Ezekieli 7:27

Ezekieli 7:27 CCL

Mfumu idzalira, kalonga adzagwidwa ndi mantha. Manja a anthu a mʼdzikomo azidzangonjenjemera ndi mantha. Ine ndidzawalanga molingana ndi machitidwe awo, ndipo ndidzawaweruza molingana ndi momwe anaweruzira anzawo. Choncho adzadziwa kuti Ine ndine Yehova.”