YouVersion Logo
Search Icon

Ezekieli 37:7-8

Ezekieli 37:7-8 CCL

Ndipo ndinanenera monga anandilamulira. Ndipo pamene ndinkanenera, ndinamva gobedegobede, ndipo mafupa aja anayamba kulumikizana, fupa ku fupa linzake. Ine ndinayangʼana, ndipo mitsempha ndi mnofu zinabwera pa mafupawo ndipo khungu linaphimba pamwamba pake, koma munalibe mpweya mwa iwo.

Free Reading Plans and Devotionals related to Ezekieli 37:7-8