YouVersion Logo
Search Icon

Ezekieli 33:9

Ezekieli 33:9 CCL

Koma ngati uchenjeza munthu woyipa kuti aleke njira zake, ndipo iye osatero, adzafa chifukwa cha tchimo lake, koma iwe udzapulumutsa moyo wako.

Free Reading Plans and Devotionals related to Ezekieli 33:9