YouVersion Logo
Search Icon

Ezekieli 33:6

Ezekieli 33:6 CCL

Koma ngati mlondayo aona lupanga likubwera ndipo osawomba lipengalo kuchenjeza anthu, ndipo lupanga libwera ndi kuchotsa moyo wa mmodzi mwa iwo, munthu ameneyo adzafa chifukwa cha tchimo lake, koma ndidzamuyimba mlandu mlondayo chifukwa cha imfa ya mnzakeyo.’

Free Reading Plans and Devotionals related to Ezekieli 33:6