Bible App logo
Search Icon

Ezekieli 3:19

Ezekieli 3:19 CCL

Koma ukamuchenjeza munthu woyipa koma iye osatembenuka mtima kuleka zoyipa zake kapena kusiya njira zake zoyipa, munthuyo adzafa chifukwa cha uchimo wake koma iwe udzapulumutsa moyo wako.

Free Reading Plans and Devotionals related to Ezekieli 3:19