Bible App logo
Search Icon

Ezekieli 2:7-8

Ezekieli 2:7-8 CCL

Ukawawuze ndithu mawu anga, kaya akamva kaya sakamva. Paja anthuwa ndi awupandu. Koma iwe mwana wa munthu, mvetsera zimene ndikukuwuza. Usakhale wowukira ngati iwowo. Tsono yasama pakamwa pako kuti udye chimene ndikukupatsa.”

Free Reading Plans and Devotionals related to Ezekieli 2:7-8