Ezekieli 17:24
Ezekieli 17:24 CCL
Mitengo yonse yakuthengo idzadziwa kuti Ine ndine Yehova amene ndimafupikitsa mitengo yayitali ndi kutalikitsa mitengo yayifupi. Ndimawumitsa mitengo yabiriwiri ndi kubiriwitsa mitengo yowuma. “ ‘Ine Yehova ndayankhula zimenezi, ndipo ndidzazichita.’ ”


