YouVersion Logo
Search Icon

Eksodo 7:11-12

Eksodo 7:11-12 CCL

Naye Farao anayitanitsa anthu ake anzeru ndi amatsenga, ndipo nawonso amatsenga a Chiigupto anachita zinthu zomwezo mwa matsenga awo. Aliyense wa iwo anaponya ndodo yake pansi ndipo inasanduka njoka. Koma ndodo ya Aaroni inameza ndodo zawo.

Free Reading Plans and Devotionals related to Eksodo 7:11-12