YouVersion Logo
Search Icon

Eksodo 6:6

Eksodo 6:6 CCL

“Nʼchifukwa chake nena kwa Aisraeli kuti, ‘Ine ndine Yehova, ndipo ndidzakutulutsani mʼgoli la Aigupto. Ndidzakumasulani mu ukapolo, ndidzakuwombolani ndi dzanja langa lotambasuka ndi kuchita ntchito zachiweruzo.

Free Reading Plans and Devotionals related to Eksodo 6:6