YouVersion Logo
Search Icon

Eksodo 6:1

Eksodo 6:1 CCL

Yehova anawuza Mose kuti, “Tsopano udzaona zimene ndimuchite Farao: Chifukwa cha dzanja langa lamphamvu adzalola anthu anga kuti atuluke. Chifukwa cha dzanja langa lamphamvu adzawatulutsa mʼdziko lake.”

Free Reading Plans and Devotionals related to Eksodo 6:1