YouVersion Logo
Search Icon

Eksodo 5:2

Eksodo 5:2 CCL

Koma Farao anati, “Yehova ndani kuti ine ndimumvere ndi kulola Aisraeli kuti apite? Ine Yehova sindikumudziwa ndipo sindilola kuti Aisraeli apite.”

Free Reading Plans and Devotionals related to Eksodo 5:2