YouVersion Logo
Search Icon

Eksodo 35:30-31

Eksodo 35:30-31 CCL

Kenaka Mose anati kwa Aisraeli, “Taonani, Yehova wasankha Bezaleli mwana wa Uri, mwana wa Huri, wa fuko la Yuda, ndipo wamudzaza ndi Mzimu wa Mulungu kotero kuti ali ndi luso ndi nzeru zomvetsa zinthu, ndipo akudziwa bwino ntchito zonse zamanja monga izi

Free Reading Plans and Devotionals related to Eksodo 35:30-31