YouVersion Logo
Search Icon

Eksodo 34:10

Eksodo 34:10 CCL

Choncho Yehova anati: “Ine ndikuchita nanu pangano. Ndidzachita zodabwitsa pamaso pa anthu onse zimene sizinachitikenso ndi mtundu wina uliwonse wa anthu pa dziko lonse lapansi. Anthu amene mudzakhala pakati pawo adzaona kuopsa kwa ntchito imene Ine Yehova ndidzakuchitireni.

Free Reading Plans and Devotionals related to Eksodo 34:10