YouVersion Logo
Search Icon

Eksodo 32:30

Eksodo 32:30 CCL

Mmawa mwake Mose anati kwa anthu onse, “Inu mwachita tchimo lalikulu. Koma tsopano ine ndipita ku phiri kwa Yehova mwina ndikatha kukupepeserani chifukwa cha tchimo lanu.”

Free Reading Plans and Devotionals related to Eksodo 32:30