Eksodo 29:45-46
Eksodo 29:45-46 CCL
Ndidzakhala pakati pa Aisraeli ndikukhala Mulungu wawo. Adzadziwa kuti ine ndine Mulungu wawo amene ndinawatulutsa mʼdziko la Igupto kuti ndikhale pakati pawo. Ine ndine Yehova, Mulungu wawo.”
Ndidzakhala pakati pa Aisraeli ndikukhala Mulungu wawo. Adzadziwa kuti ine ndine Mulungu wawo amene ndinawatulutsa mʼdziko la Igupto kuti ndikhale pakati pawo. Ine ndine Yehova, Mulungu wawo.”