YouVersion Logo
Search Icon

Eksodo 28:4

Eksodo 28:4 CCL

Zovala zoti apange ndi izi: chovala chapachifuwa, efodi, mkanjo, mwinjiro wolukidwa, nduwira ndi lamba. Apangire mʼbale wako Aaroni ndi ana ake aamuna zovala zopatulikazi kuti iwo anditumikire monga ansembe.

Free Reading Plans and Devotionals related to Eksodo 28:4