YouVersion Logo
Search Icon

Eksodo 28:3

Eksodo 28:3 CCL

Uwawuze anthu onse aluso amene Ine ndawapatsa nzeru pa ntchito yosoka kuti apange zovala za Aaroni za pa mwambo womupatula, kuti iye anditumikire monga wansembe.

Free Reading Plans and Devotionals related to Eksodo 28:3