YouVersion Logo
Search Icon

Eksodo 16:8

Eksodo 16:8 CCL

Mose anati, “Yehova adzakupatsani nyama madzulo aliwonse ndi buledi mmawa uliwonse kuti mukhute chifukwa Iye wamva madandawulo anu. Nanga ife ndi yani? Kudandaula kwanu simudandaulira ife, koma Yehova.”

Free Reading Plans and Devotionals related to Eksodo 16:8