YouVersion Logo
Search Icon

Eksodo 15:11

Eksodo 15:11 CCL

Ndithu Yehova, pakati pa milungu, ndani afanana nanu? Inu amene muli woyera, ndiponso wotamandika wolemekezeka, chifukwa cha ntchito zanu, zazikulu ndi zodabwitsa?

Free Reading Plans and Devotionals related to Eksodo 15:11