YouVersion Logo
Search Icon

Eksodo 1:17

Eksodo 1:17 CCL

Koma azambawo ankaopa Mulungu ndipo sanachite zimene mfumu ya Igupto inawawuza kuti achite. Iwo analeka ana aamuna kuti akhale ndi moyo.

Free Reading Plans and Devotionals related to Eksodo 1:17