YouVersion Logo
Search Icon

Mlaliki 8:14

Mlaliki 8:14 CCL

Palinso chinthu china chopanda phindu chomwe chimachitika pa dziko lapansi: anthu olungama amalangidwa ngati anthu osalungama. Pamene oyipa amalandira zabwino ngati kuti ndi anthu abwino.

Free Reading Plans and Devotionals related to Mlaliki 8:14