YouVersion Logo
Search Icon

Mlaliki 8:12

Mlaliki 8:12 CCL

Ngakhale munthu woyipa apalamule milandu yambirimbiri, nʼkumakhalabe ndi moyo wautali, ine ndikudziwa kuti anthu owopa Mulungu zinthu zidzawayendera bwino, omwe amapereka ulemu pamaso pa Mulungu.

Free Reading Plans and Devotionals related to Mlaliki 8:12