YouVersion Logo
Search Icon

Mlaliki 7:14

Mlaliki 7:14 CCL

Pamene zinthu zili bwino, sangalala; koma pamene zinthu sizili bwino, ganizira bwino: Mulungu ndiye anapanga nthawi yabwinoyo, ndiponso nthawi imene si yabwinoyo. Choncho munthu sangathe kuzindikira chilichonse cha mʼtsogolo mwake.

Free Reading Plans and Devotionals related to Mlaliki 7:14