YouVersion Logo
Search Icon

Mlaliki 6:2

Mlaliki 6:2 CCL

Mulungu amapereka chuma, zinthu ndi ulemu kwa munthu, kotero kuti munthuyo sasowa kanthu kalikonse kamene akukalakalaka, koma Mulungu samulola kuti adyerere zinthuzo, ndipo mʼmalo mwake amadyerera ndi mlendo. Izi ndi zopandapake, ndi zoyipa kwambiri.

Free Reading Plans and Devotionals related to Mlaliki 6:2