YouVersion Logo
Search Icon

Mlaliki 5:19

Mlaliki 5:19 CCL

Komatu pamene Mulungu apereka chuma kwa munthu aliyense ndi zinthu zina, ndi kulola kuti akondwere ndi chumacho, munthuyo alandire chumacho ndi kusangalala ndi ntchito yake, imene ndi mphatso yochokera kwa Mulungu.

Free Reading Plans and Devotionals related to Mlaliki 5:19