YouVersion Logo
Search Icon

Mlaliki 4:4

Mlaliki 4:4 CCL

Ndipo ndinazindikira kuti ntchito zonse zolemetsa ndiponso ntchito zonse zaluso zimachitika chifukwa choti wina akuchitira nsanje mnzake. Izinso ndi zopandapake, nʼkungodzivuta chabe.

Free Reading Plans and Devotionals related to Mlaliki 4:4