YouVersion Logo
Search Icon

Mlaliki 3:7-8

Mlaliki 3:7-8 CCL

Nthawi yongʼamba ndi nthawi yosoka, nthawi yokhala chete ndi nthawi yoyankhula. Nthawi yokondana ndi nthawi yodana, nthawi ya nkhondo ndi nthawi ya mtendere.

Free Reading Plans and Devotionals related to Mlaliki 3:7-8