YouVersion Logo
Search Icon

Mlaliki 12:1-2

Mlaliki 12:1-2 CCL

Uzikumbukira mlengi wako masiku a unyamata wako, masiku oyipa asanafike, nthawi isanafike pamene udzanena kuti, “Izi sizikundikondweretsa.” Nthawi ya ukalamba wako, dzuwa ndi kuwala, mwezi ndi nyenyezi zidzada. Mitambo idzabweranso mvula itagwa.

Free Reading Plans and Devotionals related to Mlaliki 12:1-2