YouVersion Logo
Search Icon

Danieli 7:14

Danieli 7:14 CCL

Anapatsidwa ulamuliro, ulemerero ndi mphamvu za ufumu kuti anthu a mitundu ina yonse, mayiko ndi anthu aziyankhulo zosiyanasiyana apembedze iye. Mphamvu zake ndi mphamvu zamuyaya zimene sizidzatha, ndipo ufumu wake sudzawonongeka konse.

Free Reading Plans and Devotionals related to Danieli 7:14