YouVersion Logo
Search Icon

Amosi 4:13

Amosi 4:13 CCL

Iye amene amawumba mapiri, amalenga mphepo, ndipo amawululira munthu za mʼmaganizo ake, Iye amene amasandutsa usana kuti ukhale mdima, ndipo amayenda pa zitunda za dziko lapansi, dzina lake ndi Yehova Mulungu Wamphamvuzonse.

Free Reading Plans and Devotionals related to Amosi 4:13