YouVersion Logo
Search Icon

Amosi 2:4

Amosi 2:4 CCL

Yehova akuti, “Chifukwa anthu a ku Yuda akunka nachimwirachimwira, Ine sindileka kuwalanga. Popeza iwo akana lamulo la Yehova ndipo sanasunge malangizo ake, popeza asocheretsedwa ndi milungu yabodza, milungu imene makolo awo ankayitsatira,

Free Reading Plans and Devotionals related to Amosi 2:4