YouVersion Logo
Search Icon

AROMA 6:4

AROMA 6:4 BLP-2018

Chifukwa chake tinaikidwa m'manda pamodzi ndi Iye mwa ubatizo kulowa muimfa; kuti monga Khristu anaukitsidwa kwa akufa mwa ulemerero wa Atate, chotero ifenso tikayende m'moyo watsopano.

Free Reading Plans and Devotionals related to AROMA 6:4