YouVersion Logo
Search Icon

AROMA 4:20-21

AROMA 4:20-21 BLP-2018

ndipo poyang'anira lonjezo la Mulungu sanagwedezeke chifukwa cha kusakhulupirira, koma analimbika m'chikhulupiriro, napatsa Mulungu ulemu, nakhazikikanso mumtima kuti, chimene Iye analonjeza, anali nayonso mphamvu yakuchichita.

Free Reading Plans and Devotionals related to AROMA 4:20-21