YouVersion Logo
Search Icon

AROMA 4:18

AROMA 4:18 BLP-2018

Amene anakhulupirira nayembekeza zosayembekezeka, kuti iye akakhale kholo la mitundu yambiri ya anthu, monga mwa chonenedwachi, Mbeu yako idzakhala yotere.

Free Reading Plans and Devotionals related to AROMA 4:18