YouVersion Logo
Search Icon

MATEYU 5:15-16

MATEYU 5:15-16 BLP-2018

Kapena sayatsa nyali, ndi kuivundikira m'mbiya, koma aiika iyo pa choikapo chake; ndipo iunikira onse ali m'nyumbamo. Chomwecho muwalitse inu kuunika kwanu pamaso pa anthu, kuti pakuona ntchito zanu zabwino, alemekeze Atate wanu wa Kumwamba.

Free Reading Plans and Devotionals related to MATEYU 5:15-16