YouVersion Logo
Search Icon

MATEYU 5:13

MATEYU 5:13 BLP-2018

Inu ndinu mchere wa dziko lapansi; koma mcherewo ngati ukasukuluka, adzaukoleretsa ndi chiyani? Pamenepo sungakwanirenso kanthu konse, koma kuti ukaponyedwe kunja, nupondedwe ndi anthu.

Free Reading Plans and Devotionals related to MATEYU 5:13