YouVersion Logo
Search Icon

MATEYU 24:9-11

MATEYU 24:9-11 BLP-2018

Pamenepo adzakuperekani kunsautso, nadzakuphani; ndipo anthu a mitundu yonse adzadana nanu, chifukwa cha dzina langa. Ndipo pomwepo ambiri adzakhumudwa, nadzaperekana wina ndi mnzake, nadzadana wina ndi mnzake. Ndipo aneneri onama ambiri adzauka, nadzasokeretsa anthu ambiri.

Free Reading Plans and Devotionals related to MATEYU 24:9-11