Bible App logo
Search Icon

MATEYU 11:4-5

MATEYU 11:4-5 BLP-2018

Ndipo Yesu anayankha, nanena nao, Mukani mubwezere mau kwa Yohane zimene muzimva ndi kuziona: akhungu alandira kuona kwao, ndi opunduka miyendo ayenda, akhate akonzedwa, ndi ogontha akumva, ndi akufa aukitsidwa, ndi kwa aumphawi ulalikidwa Uthenga Wabwino.

Free Reading Plans and Devotionals related to MATEYU 11:4-5