YouVersion Logo
Search Icon

MATEYU 1:20

MATEYU 1:20 BLP-2018

Koma pakusinkhasinkha iye zinthu izi, onani, mngelo wa Ambuye anaonekera kwa iye m'kulota, nanena, Yosefe, mwana wa Davide, usaope kudzitengera wekha Maria mkazi wako; pakuti icho cholandiridwa mwa iye chili cha Mzimu Woyera.

Free Reading Plans and Devotionals related to MATEYU 1:20