YouVersion Logo
Search Icon

GENESIS 22:9

GENESIS 22:9 BLP-2018

Ndipo anafika kumalo komwe Mulungu anamuuza iye; ndipo Abrahamu anamanga guwa la nsembe nakonza nkhuni, namanga Isaki mwana wake, namuika iye paguwa la nsembe pamwamba pa nkhuni.

Free Reading Plans and Devotionals related to GENESIS 22:9