YouVersion Logo
Search Icon

MACHITIDWE 7:57-58

MACHITIDWE 7:57-58 BLP-2018

Koma anafuula ndi mau aakulu, natseka m'makutu mwao, namgumukira iye ndi mtima umodzi; ndipo anamtaya kunja kwa mzinda, namponya miyala; ndipo mbonizo zinaika zovala zao pa mapazi a mnyamata dzina lake Saulo.

Free Reading Plans and Devotionals related to MACHITIDWE 7:57-58