1
Matayo 8:26
Nyanja
NTNYBL2025
Yesu wadaayangha, “Imwe wandhu achikulupi chochepa, ndandeyanji muopa?” Yesu wadaima nukutuliza mwela ni nyanja idagona.
Compare
Explore Matayo 8:26
2
Matayo 8:8
Nambho yujha wamkulu waloma wadamkambila, “Imwe Ambuye, ine sinifunika imwe mulowe mnyumba mwanga, nambho chochani lamulope, ni mbowa wanga siwalame.
Explore Matayo 8:8
3
Matayo 8:10
Yesu yapo wadavela chimwecho, wadazizwa, wadaakambila wandhu wajha adamchata, “Zene nikukambilani, sinidaone mundhu waliyonjhe mujhiko la Izilaeli uyo wali ni chikhulupi ngati ichi.
Explore Matayo 8:10
4
Matayo 8:13
Ndiipo Yesu wadamkambila yujha wamkulu wa Loma, “Pita kukhomo, ni ikhale ngati umo wakhulupilila.” Ni mbowa wake wadalama saa imweijha.
Explore Matayo 8:13
5
Matayo 8:27
Wandhu adadabwa, adajhifunjha, “Mundhu wabwanji uyu? Ata mbhepo ni mafunde vimvela!”
Explore Matayo 8:27
Home
Bible
Plans
Videos