1
Matayo 5:15-16
Nyanja
NTNYBL2025
Wandhu saakweleza nyali ni kuikupika kwa debe. Nambho iyikidwa pamwamba poikila nyali kuti imulikile wandhu wonjhe yao ali mnyumba. Chimwecho dangalila lanu liwale pamaso pa wandhu kuti apenye vichito vanu vabwino ni kwaakweza Atate wanu akumwamba.”
Compare
Explore Matayo 5:15-16
2
Matayo 5:14
“Anyiimwe ni dangalila la jhiko! Ni ngati nyumba iyo yamangidwa pamwamba pa phili siukhoza kubisika.
Explore Matayo 5:14
3
Matayo 5:8
“Ali ni mwawi yao ali ni mtima wabwino pakuti saamuone Mnungu.”
Explore Matayo 5:8
4
Matayo 5:6
“Ali ni mwawi yao afuna kupunda kuchita ivo vimkwadilicha Mnungu ndande Mnungu siwatangatile kuchita chimwecho.”
Explore Matayo 5:6
5
Matayo 5:44
Nambho ine nikukambilani akondeni adani wanu ni kwapembhela anyiyao akuvutichani anyiimwe
Explore Matayo 5:44
6
Matayo 5:3
“Ali ni mwawi wajha ajhiwa kuti amfuna Mnungu pakuti ufumu wa kumwamba ni wao.”
Explore Matayo 5:3
7
Matayo 5:9
“Ali ni mwawi wajha apeleka mtendele pakuti siatanidwe wana a Mnungu.”
Explore Matayo 5:9
8
Matayo 5:4
“Ali ni mwawi yao ali ni chisoni pakuti siathilidwe mtima.”
Explore Matayo 5:4
9
Matayo 5:10
“Ali ni mwayi anyiyao avutichidwa ndande ya kuchita yayo wafuna Mnungu Pakuti ufumu wa kumwamba ni wao!”
Explore Matayo 5:10
10
Matayo 5:7
“Ali ni mwawi wajha alengela wina lisungu pakuti Mnungu siwalengele lisungu.”
Explore Matayo 5:7
11
Matayo 5:11-12
“Muli ni mwawi wandhu yapo sakutukwaneni ni kukuvutichani ni kukunamizilani voipa ndande yanga. Kondwani ni lulutilani pakuti chikho chanu chachikulu chaikidwa kumwamba. Mchimwecho nde umo adaavuticha alosi akhale anyiimwe mkali wosabdwa.”
Explore Matayo 5:11-12
12
Matayo 5:5
“Ali ni mwawi yao ajhichicha pakuti Mnungu siwapache jhiko likhale lao.”
Explore Matayo 5:5
13
Matayo 5:13
“Anyiimwe ni mchele wa chinyope wa jhiko. Nambho mchele wa chinyopeo ngati wasukuluka sikomelechedwe ni chiyani? Ulibe njhito. Siutaidwe kubwalo nikupondedwa ni wandhu.”
Explore Matayo 5:13
14
Matayo 5:48
Chimwecho khalani wokwanila ngati Tate wanu wa kumwamba umo wali okwanila.”
Explore Matayo 5:48
15
Matayo 5:37
Ukakamba, ‘Yetu’ basi ikhale ‘Yetu.’ Ukakamba, ‘Notho’ basi ikhale ‘Notho.’ Chalichonjhe icho chipitilila nghani zimenezo chichoka kwa Woyesa.”
Explore Matayo 5:37
16
Matayo 5:38-39
“Mwavela kuti idakambidwa, ‘Diso kwa diso ni jhino kwa jhino.’ Nambho ine nikukambilani, msadabwezela mbwezo kwa mundhu uyo wakuchitila voipa. Mundhu wakakubula mbama kuchakaya la kwene chinchijha mleke wakubule chakaya lakawili.
Explore Matayo 5:38-39
17
Matayo 5:29-30
Ngati diso lako la kwene likakuchiticha kuti uchite chimo lizule ni kulitaya kutali. Mbasa kutaiza chiwalo chimojhi cha thupi lako kusiyana ni thupi lako lonjhe kutaidwa ku jehanamu ya moto. Ngati jhanja lako la kwene likuchiticha kuti uchite chimo lidule ni ukalitaye kutali ni iwe. Mbasa kutaiza chiwalo chimojhi cha thupi lako kusiyana ni thupi lako lonjhe kutaidwa ku jehanamu ya moto.”
Explore Matayo 5:29-30
Home
Bible
Plans
Videos