1
Luka 16:10
Nyanja
NTNYBL2025
Waliyonjhe uyo wakhoza kukhulupika pavindhu vochepa kupunda, siwakhoze kukhulupilika kwa vindhu vavikulu. Waliyonjhe uyo siwakhulupika pa vindhu vochepa siwakhulipilika pa vindhu vavikulu.
Compare
Explore Luka 16:10
2
Luka 16:13
Palibe kapolo uyo wakhoza kutumikila wakulu awili kwa ndhawi imojhi. Pakuti siwamuipile mmojhi wao ni kumkonda mnjake, kapina siwagwilizane ni mmojhi ni kumdelela mnjake. Chemwecho, simngakhoze kumtumikila Mnungu ni ndalama vonjhe pamojhi.
Explore Luka 16:13
3
Luka 16:11-12
Chimwecho, ngati siudakhale okhulupilika pakutumila chuma chapajhiko lapanjhi, yani uyo siwakukhulupilileni kukupachani chuma cha uzimu? Ni ngati simukhulupilka pachuma cha mundhu wina, yani uyo siwakupacheni chuma icho chili chanu mwachiwene wake?
Explore Luka 16:11-12
4
Luka 16:31
Ndiipo Ibulahimu wadamuyangha, ‘Ngati sayavela mathauko ya Musa pamojhi ni malembo ya alosi, sangakhoze kuvela ata ngati wakapitila mmojhi uyo wahyuka kuchokela kwa akufa.’”
Explore Luka 16:31
5
Luka 16:18
Waliyonjhe uyo wamsiya mkazake ni kukwata wamkazi mwina, wachita chogololo. Ni wammuna uyo wamkwata wamkazi uyo wasiyidwa ni mmunake, wachitanayo chigololo.
Explore Luka 16:18
Home
Bible
Plans
Videos