1
Zek. 2:5
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
BLY-DC
Chauta akuti Iye yemwe ndiye adzakhale linga lamoto loteteza mzindawo, ndipo adzaonetsa ulemerero wake m'kati mwake.”
Compare
Explore Zek. 2:5
2
Zek. 2:10
“Inu anthu a ku Ziyoni, imbani mokondwa, chifukwa ndikubwera, ndikudzakhala pakati panu,” akutero Chauta.
Explore Zek. 2:10